2 Corinthians 6:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malo sakusoŵani mumtima mwathu, koma mumtima mwanu ndimo mukusoŵa malo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Simupsinjika mwa ife, koma mupsinjika mumtima mwanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ife sitikukubisirani chikondi chathu pa inu, koma inu mukubisa chikondi chanu pa ife.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Simupsinjika mwa ife, koma mupsiniika mumtima mwanu.