2 Corinthians 7:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikukondwa kuti ndingathe kukukhulupirirani pa zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndikondwera kuti m'zonse ndilimbika mtima za inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndine wokondwa kuti ndingathe kukukhulupirirani pa zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndikondwera kuti m'zonse ndilimbika mtima za inu.