2 Corinthians 8:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sindikufuna kunena kuti inuyo muvutike, ena apepukidwe, ai, koma kuti pakhale kulingana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti sinditero kuti ena akamasuke, ndi inu musautsidwe;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Cholinga chathu sikuti tipeputse ena pamene inuyo mukuvutika, koma kuti pakhale kufanana.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti sinditero kuti ena akamasuke, ndi inu musautsidwe;