2 Corinthians 8:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tiyamike Mulungu kuti adaika mumtima mwa Tito changu chomwecho chimene ife tili nacho pokuthandizani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ayamikike Mulungu, wakupatsa khama lomweli la kwa inu mu mtima wa Tito.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tithokoze Mulungu amene anayika mu mtima wa Tito changu chomwecho chimene ine ndili nacho pa inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ayamikike Mulungu, wakupatsa khama lomweli la kwa inu mu mtima wa Tito.