2 John 1:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a mbale wanu wosankhidwa ndi Mulungu akuti moni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akupereka moni ana a mbale wanu wosankhika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a mlongo wanu wosankhidwa ndi Mulungu akupereka moni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akulankhulani ana a mbale wanu wosankhika.