2 Kings 15:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Salumu mwana wa Yabesi adaloŵa ufumu pa chaka cha 39 cha ufumu wa Uziya mfumu ya ku Yuda, ndipo adalamulira mwezi umodzi ku Samariya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Salumu mwana wa Yabesi analowa ufumu wake chaka cha makumi atatu mphambu zisanu ndi zinai cha Uziya mfumu ya Yuda, nakhala mfumu mwezi umodzi m'Samariya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Salumu mwana wa Yabesi anakhala mfumu mʼchaka cha 39 cha ulamuliro wa Uziya mfumu ya Yuda ndipo analamulira mu Samariya mwezi umodzi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Salumu mwana wa Yabesi analowa ufumu wace caka ca makumi atatu mphambu zisanu ndi zinai ca Uziya mfumu ya Yuda, nakhala mfumu mwezi umodzi m'Samariya.