2 Kings 15:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Azariya adachita zolungama pamaso pa Chauta, monga momwe ankachitira bambo wake Amaziya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iyeyo anachita zabwino pamaso pa Yehova, monga momwe anachitira Amaziya abambo ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nacita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazicita atate wace Amaziya.