2 Kings 15:37 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthaŵi imene Yotamu ankalamulira, mpamene Chauta adayambapo kutuma Rezini mfumu ya ku Siriya ndi Peka mwana wa mfumu ya ku Israele, kuti akathire nkhondo dziko la Yuda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Masiku awa Yehova anayamba kutumizira Yuda Rezini mfumu ya Aramu, ndi Peka mwana wa Remaliya, amenyane naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
(Nthawi imeneyo, Yehova anayamba kumatuma Rezini mfumu ya Aaramu ndi Peka mwana wa Remaliya kudzamenyana ndi Yuda).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Masiku awa Yehova anayamba kutumizira Yuda Rezini mfumu ya Aramu, ndi Peka mwana wa Remaliya, amenyane naye.