2 Kings 17:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero mmodzi mwa ansembe amene adaŵatenga ku Samariya adadzakhala ku Betele, nayamba kuŵaphunzitsa anthu kupembedza Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nadza wina wa ansembewo adawachotsa ku Samariya, nakhala ku Betele, nawalangiza m'mene azimuopera Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho mmodzi mwa ansembe amene anawatenga ku Samariya anabwera kudzakhala ku Beteli ndipo ankaphunzitsa anthuwo kupembedza Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nadza wina wa ansembewo adawacotsa ku Samariya, nakhala ku Beteli, nawalangiza m'mene azimuopera Yehova.