2 Kings 2:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lina anthu amumzinda adauza Elisa kuti, “Onani, mzinda wathuwu ngwabwino kwambiri, zonse zili bwino monga mukuwoneramu, koma madzi okha ngoipa, ndipo nthaka yake njosabereka.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo amuna akumudzi anati kwa Elisa, Taonani, pamudzi pano mpabwino, monga umo aonera mbuye wanga; koma madzi ndi oipa, ndi nthaka siibalitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a mu mzindamo anati kwa Elisa, “Mbuye wathu, taonani mzinda uno uli pamalo pabwino, monga mukuoneramu, koma madzi ake ndi oyipa, nthaka yakenso ndi yosabereka.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo amuna a kumudzi anati kwa Elisa, Taonani, pamudzi pano mpabwino, monga umo aonera mbuye wanga; koma madzi ndi oipa, ndi nthaka siibalitsa.