2 Kings 20:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pomwepo Hezekiya adatembenuka nayang'ana ku khoma, nayamba kupemphera kwa Chauta kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo anatembenuzira nkhope yake kukhoma, napemphera kwa Yehova, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Hezekiya anatembenuka nayangʼana ku khoma ndipo anapemphera kwa Yehova kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo anatembenuzira nkhope yace kukhoma, napemphera kwa Yehova, ndi kuti,