2 Kings 21:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adakana Chauta, Mulungu wa makolo ake, ndipo sadamvere malamulo ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nasiya Yehova Mulungu wa makolo ake, sanayende m'njira ya Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iyeyo anasiya Yehova Mulungu wa makolo ake ndipo sanayende mʼnjira ya Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nasiya Yehova Mulungu wa makolo ace, sanayenda m'njira ya Yehova.