2 Kings 21:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atamwalira adaikidwa m'manda m'munda wa ku nyumba yake, m'munda wa Uza. Ndipo mwana wake Yosiya adaloŵa ufumu m'malo mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Naikidwa iye m'manda mwake m'munda wa Uza; nakhala mfumu m'malo mwake Yosiya mwana wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anayikidwa mʼmanda ake mʼmunda wa Uza. Ndipo Yosiya mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Naikidwa iye m'manda mwace m'munda wa Uza; nakhalamfumum'malo mwace Yosiya mwana wace.