2 Kings 25:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono mkulu wa asilikali uja adagwira Seraya mkulu wa nsembe ndi Zefaniya wachiŵiri kwa mkulu wa ansembe, ndi alonda atatu apakhomo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mkulu wa olindirira anatenga Seraya wansembe wamkulu, ndi Zefaniya wansembe wachiwiri, ndi olindira pakhomo atatu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mkulu wa asilikali uja anagwira ukapolo mkulu wa ansembe Seraya, Zefaniya wachiwiri wa mkulu wa ansembe ndi alonda atatu apakhomo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mkuru wa olindirira anatenga Seraya wansembe wamkulu, ndi Zefaniya wansembe waciwiri, ndi olindira pakhomo atatu;