2 Kings 4:36 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pomwepo Elisa adaitana Gehazi nati, “Muitane mai uja.” Iye adamuitana maiyo. Ndipo atabwera, Elisayo adati, “Nayu mwana wanu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo anaitana Gehazi, nati, Kaitane Msunamu uja. Namuitana. Ndipo atalowa kuli iye, anati, Nyamula mwana wako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Elisa anayitana Gehazi ndipo anati, “Muyitane Msunemuyo.” Ndipo anaterodi. Mayiyo atabwera, Elisa anati, “Tenga mwana wako.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo anaitana Gehazi, nati, Kaitane Msunemu uja, Namuitana. Ndipo atalowa kuli iye, anati, Nyamula mwana wako.