2 Kings 8:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iyeyonso ankatsata chitsanzo choipa cha banja la Ahabu. Adachita zoipa pamaso pa Chauta monga m'mene linkachitira banja la Ahabu, poti anali mkamwini m'banja la Ahabu lomwelo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anayenda m'njira ya nyumba ya Ahabu, nachita choipa pamaso pa Yehova, m'mene inachitira nyumba ya Ahabu; pakuti ndiye wa chibale cha banja la Ahabu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anatsatira makhalidwe a banja la Ahabu ndipo anachita zoyipa pamaso pa Yehova, monga linachitira banja la Ahabu, pakuti anali mkamwini wa banja la Ahabu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anayenda m'njira ya nyumba ya Ahabu, nacita coipa pamaso pa Yehova, m'mene inacitira nyumba ya Ahabu; pakuti ndiye wa cibale ca banja la Ahabu.