2 Peter 1:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakuti ndikudziŵa kuti nthaŵi yakutuluka mu msasa wanga uno yayandikira, monga andidziŵitsira Ambuye athu Yesu Khristu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
podziwa kuti kuleka kwa msasa wanga kuli pafupi, monganso Ambuye wathu Yesu Khristu anandilangiza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
chifukwa ndikudziwa kuti posachedwapa ndikuchoka mu msasa uno, monga Ambuye athu Yesu Khristu anandidziwitsiratu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
podziwa kuti kuleka kwa msasa wanga kuli pafupi, monganso Ambuye wathu Yesu Kristu anandilangiza.