2 Peter 3:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zindikirani kuti Ambuye athu akukulezerani mtima kuti mupulumuke. Paulo, mbale wathu wokondedwa uja, nayenso adakulemberani za zimenezi ndi nzeru zimene Mulungu adampatsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo yesani kulekerera kwa Ambuye wathu chipulumutso; monganso mbale wathu wokondedwa Paulo, monga mwa nzeru zopatsidwa kwa iye, anakulemberani;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zindikirani kuti kuleza mtima kwa Ambuye kukutanthauza chipulumutso, monga momwe mʼbale wathu wokondedwa Paulo anakulemberaninso ndi nzeru zimene Mulungu anamupatsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo yesani kulekerera kwa Ambuye wathu cipulumutso; monganso mbale wathu wokondedwa Paulo, monga mwa nzeru zopatsidwa cwa iye, anakulemberani;