2 Peter 3:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo ndi madzi okhaokhawo dziko lapansi la masiku amenewo lidamizidwa ndi kuwonongedwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
mwa izi dziko lapansi la masiku aja, pomizika ndi madzi, lidaonongeka;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndi madzinso achigumula, dziko lapansi la masiku amenewo linawonongedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
mwa izi dziko lapansi la masiku aja, pomizika ndi madzi, lidaonongeka;