2 Samuel 1:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Davide adamufunsanso kuti, “Nanga iwe sudachite mantha bwanji kutambalitsa dzanja lako nkupha wodzozedwa wa Chauta?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Davide ananena naye, Bwanji sunaopa kusamula dzanja lako kuononga wodzozedwa wa Yehova?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Davide anamufunsanso kuti, “Nʼchifukwa chiyani sunaope kukweza dzanja lako ndi kupha wodzozedwa wa Yehova?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Davide ananena naye, Bwanji sunaopa kusamula dzanja lako kuononga wodzozedwa wa Yehova?