2 Samuel 1:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo Davide adati, “Wadziphetsa wekha, unanena wekha ndi pakamwa pako kuti, ‘Ndidapha wodzozedwa wa Chauta.’ ”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma asanafe, Davide adanena naye, Wadziphetsa ndi mtima wako; chifukwa pakamwa pako padachita umboni wakukutsutsa ndi kuti, Ine ndinapha wodzozedwa wa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti Davide anali atanena kwa iye kuti, “Iwe wadzipha wekha. Pakamwa pako pakunena zokutsutsa wekha, pamene unanena kuti, ‘Ine ndapha wodzozedwa wa Yehova.’ ”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma asanafe, Davide adanena naye, Wadziphetsa ndi mtima wako; cifukwa pakamwa pako padacita umboni wakukutsutsa ndi kuti, Ine ndinapha wodzozedwa wa Yehova.