2 Samuel 11:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'kalatamo adalembamo kuti, “Uriyayo umuike patsogolo penipeni pamene pakulimba nkhondo, ndipo umlekerere yekha kuti alasidwe ndi kuphedwa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi m'kalatamo analemba kuti, Mumuike Uriya pa msongwe wa nkhondo yolimba, ndipo mumlekerere kuti akanthidwe nafe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼkalatayo analembamo kuti, “Uriya mumuyike patsogolo penipeni, pamene pali nkhondo yoopsa. Ndipo mumusiye yekha kuti akanthidwe ndi kufa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi m'kalatamo analemba kuti, Mumuike Uriya pa msongwe wa nkhondo yolimba, ndipo mumlekerere kuti akanthidwe nafe.