2 Samuel 12:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pambuyo pake Chauta adatuma mneneri Natani kwa Davide. Natani atafika kwa Davide, adamphera fanizo lakuti, “Mu mzinda wina munali anthu aŵiri, wina wolemera, wina wosauka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Ndipo anafika kwa iye nanena naye, Pa mudzi wina panali anthu awiri; wina wolemera, wina wosauka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Atafika kwa Davide anati, “Panali anthu awiri mʼmizinda ina, wina wolemera ndi wina wosauka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Ndipo anafika kwa iye nanena naye, Pa mudzi wina panali anthu awiri; wina wolemera, wina wosauka.