2 Samuel 13:21 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Davide atazimva zimenezi, adapsa nazo mtima zedi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma pamene mfumu Davide anamva zonsezi, anakwiya ndithu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mfumu Davide itamva zimenezi, inakwiya kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma pamene mfumu Davide anamva zonsezi, anakwiya ndithu.