2 Samuel 15:33 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Davide adamuuza kuti, “Ukapita nane, sizindithandiza kwenikweni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Davide ananena naye, Ukapita pamodzi ndi ine udzandilemetsa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Davide anati kwa iye, “Ngati iwe upite ndi ine, udzakhala chondilemetsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Davide ananena naye, Ukapita pamodzi ndi ine udzandilemetsa;