2 Samuel 22:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adang'amba thambo natsika pansi, mdima wabii unali ku mapazi ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anaweramitsa miyambanso, natsika; ndipo mdima wandiweyani unali pansi pa mapazi ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anangʼamba thambo natsika pansi; pansi pa mapazi ake panali mitambo yakuda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anaweramitsa miyambanso, natsika; Ndipo mdima wandiwe-yani unali pansi pa mapazi ace.