2 Samuel 22:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mdima adausandutsa chofunda chake, mitambo yakuda yamvula adaisandutsa mwafuli wake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anayesa mdimawo ngati mahema omzungulira Iye, kusonkhana kwa madzi ndi mitambo yochindikira ya mlengalenga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anapanga mdima kukhala chofunda chake, mitambo yakuda ya mlengalenga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anayesa mdimawo ngati mahema omzungulira iye, Kusonkhana kwa madzi ndi mitambo yocindikira ya mlengalenga.