2 Samuel 22:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'kuŵala kumene kunali pamaso pake munkafumira makala amoto alaŵilaŵi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Cheza cha pamaso pake makala a moto anayaka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake munkachokera makala amoto alawilawi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ceza ca pamaso pace Makala a mota anayaka,