2 Samuel 22:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngalande zozama zam'nyanja zidaonekera, maziko a dziko lapansi adakhala poyera, pamene Chauta adakhuluma mokalipa, pamene adatulutsa mpweya wamphamvu m'mphuno mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo m'munsi mwa nyanja munaoneka, maziko a dziko anaonekera poyera, ndi mtonzo wa Yehova, ndi mpumo wa mpweya wa m'mphuno mwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zigwa za mʼnyanja zinaonekera poyera, ndipo maziko a dziko lapansi anakhala poyera, Yehova atabangula mwaukali, pamene mpweya wamphamvu unatuluka mʼmphuno mwake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo m'munsi mwa nyanja munaoneka, Maziko a dziko anaonekera poyera, Ndi mthonzo wa Yehova, Ndi mpumo wa mweya wa m'mphuno mwace.