2 Samuel 22:18 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adandipulumutsa kwa adani anga amphamvu, kwa onse amene ankadana nane; pakuti iwo anali amphamvu kwambiri kupambana ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, kwa iwo akudana ndi ine; pakuti anandiposa mphamvu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, adani anga amene anali amphamvu kuposa ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, Kwa iwo akudana ndi ine; pakuti anandiposa mphamvu,