2 Samuel 22:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adakandifikitsa ku malo amtendere, adandipulumutsa chifukwa adakondwera nane.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye ananditulutsanso ku malo akulu; Iye anandipulumutsa, chifukwa akondwera ndi ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anandipititsa kumalo otakasuka; anandipulumutsa chifukwa amakondwera nane.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye ananditurutsanso ku malo akuru; Iye anandipulumutsa, cifukwa akondwera ndi ine.