2 Samuel 22:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Chauta adandipatsa mphotho molingana ndi kulungama kwanga, adandifupa molingana ndi ungwiro wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova anandibwezera monga mwa cholungama changa; monga mwa kuyera kwa manja anga anandipatsa mphotho.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Yehova wandithandiza molingana ndi chilungamo changa; molingana ndi makhalidwe anga abwino, Iye wandipulumutsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova anandibwezera monga mwa colungama canga; Monga mwa kuvera kwa manja anga anandipatsa mphotho.