2 Samuel 22:24 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndinalibe mlandu pamaso pake, ndinkalewa zoipa m'moyo wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinakhalanso wangwiro kwa Iye, ndipo ndinadzisunga kusachita kuipa kwanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndakhala moyo wosalakwa pamaso pake ndipo ndakhala ndi kupewa tchimo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinakhalanso wangwiro kwa iye, Ndipo ndinadzisunga kusacita kuipa kwanga.