2 Samuel 22:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nchifukwa chake Chauta wandipatsa mphotho molingana ndi kulungama kwanga, monga momwe akuwonera kuti ndilibe mlandu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake Yehova anandibwezera monga mwa cholungama changa; monga mwa kuyera kwanga pamaso pake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova wandipatsa mphotho molingana ndi chilungamo changa, molingana ndi makhalidwe anga abwino pamaso pake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace Yehova anandibwezera monga mwa colungama canga; Monga mwa kuyera kwanga pamaso pace.