2 Samuel 22:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kwa anthu okhulupirika, Inu Mulungu mumadziwonetsa okhulupirika, kwa anthu aungwiro mumadziwonetsa abwino kotheratu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi chifundo Inu mudzadzionetsa wachifundo, ndi munthu wangwiro mudzadzionetsa wangwiro.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Kwa wokhulupirika, Inu mumaonetsa kukhulupirika kwanu, kwa anthu amakhalidwe abwino, Inu mumaonetsanso makhalidwe abwino,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi acifundo Inu mudzadzionetsa wacifundo, Ndi munthu wangwiro mudzadzionetsa wangwiro;