2 Samuel 22:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kwa anthu oyera mtima mumadziwonetsa okoma mtima, koma kwa anthu oipa mtima mumadziwonetsa ochenjera koposa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi oyera mtima mudzadzionetsa woyera mtima; ndi otsutsatsutsa mudzadzionetsa wopotoza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kwa woyera mtima, Inu mumaonetsa kuyera mtima kwanu, koma kwa anthu achinyengo mumaonetsanso kunyansidwa nawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi oyera mtima mudzadzionetsa woyera mtima; Ndi otsutsatsutsa mudzadzionetsa wopotoza.