2 Samuel 22:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndithu Inu Chauta, ndinu nyale yanga, Inu Mulungu, mumandiwunikira mu mdima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Inu ndinu nyali yanga, Yehova; ndipo Yehova adzaunika mumdima mwanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu Yehova, ndinu nyale yanga; Yehova wasandutsa mdima wanga kukhala kuwunika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Inu ndinu nyali yanga, Yehova; Ndipo Yehova adzaunika mumdima mwanga.