2 Samuel 22:34 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amalimbitsa mapazi anga ngati a mbaŵala, ndipo amandisunga bwino ku mapiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye asandutsa mapazi ake akunga mapazi a mbawala; nandiika pa misanje yanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye amasandutsa mapazi anga kukhala ngati ambawala yayikazi; Iye amandithandiza kuyimirira pamwamba pa mapiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye asandutsa mapazi ace akunga mapazi a mbawala; Nandiika pa misanje yanga.