2 Samuel 22:35 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amaphunzitsa manja anga kamenyedwe ka nkhondo, kotero kuti ndingathe kupinda uta wachitsulo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye aphunzitsa manja anga nkhondo; kotero kuti manja anga alifula uta wamkuwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; manja anga amatha kuthyola uta wachitsulo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye aphunzitsa manja anga nkhondo; Kotero kuti manja anga alifula uta wamkuwa.