2 Samuel 22:37 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwalimbitsa miyendo yanga kuti ndiyende bwino, choncho mapazi anga sadaterereke.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munakulitsa kulunza kwanga pansi panga, ndi mapazi anga sanaterereke.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu mwalimbitsa njira yanga kuti ndiyende bwino, kuti mapazi anga asaterereke.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munakulitsa kulunza kwanga pansi panga, Ndi mapazi anga sanaterereka.