2 Samuel 22:39 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidaŵakantha, ndidaŵagwetsa pansi, kotero kuti sadadzukenso, ndidaŵapondereza ndi mapazi anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinawatha ndi kuwapyoza, kuti sakhoza kuuka, inde anagwa pansi pa mapazi anga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinawakantha kotheratu, ndipo sanathe kudzukanso; Iwo anagwera pansi pa mapazi anga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinawatha ndi kuwapyoza, kuti sakhoza kuuka, Inde anagwa pansi pa mapazi anga.