2 Samuel 22:42 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adakuwa, koma panalibe ndi mmodzi yemwe woŵapulumutsa. Adalirira Chauta, koma sadaŵayankhe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anayang'ana iwo, koma panalibe wopulumutsa; ngakhale kwa Yehova, koma Iye sanawayankhe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anafuwula kupempha thandizo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe owapulumutsa. Analirira kwa Yehova, koma sanawayankhe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anayang'ana iwo, koma panalibe wopulumutsa; Ngakhale kwa Yehova, koma iye sanawayankha.