2 Samuel 22:43 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidaŵaperapera ngati fumbi, ndidaŵaphwanya ndi kuŵapondereza ngati matope amumseu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomwepo ndinawasansantha asalale ngati fumbi la padziko, ndinawapondereza ngati dothi la m'makwalala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndinawaperesa ngati fumbi la pa dziko lapansi; ndinawasinja ndipo ndinawapondaponda ngati matope a mʼmisewu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomwepo ndinawasansantha asalale ngati pfumbi la padziko, Ndinawapondereza ngati dothi la m'makwalala.