2 Samuel 22:48 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu ndiye adandithandiza kuti ndilipsire, ndi kugonjetsa anthu a mitundu ina kuti akhale mu ulamuliro wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
inde Mulungu wakundibwezera chilango ine, ndi kundigonjetsera anthu a mitundu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye ndi Mulungu amene amabwezera chilango, amene amayika anthu a mitundu yonse pansi pa ulamuliro wanga,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inde Mulungu wakundibwezera cilango ine, Ndi kundigonjetsera anthu a mitundu.