2 Samuel 22:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Zoŵaŵa za imfa zidandizinga, mitsinje ya ku malo a anthu akufa idandisefukira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti mafunde a imfa anandizinga, mitsinje ya zopanda pake inandiopsa ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Mafunde a imfa anandizinga; mitsinje yothamanga yachiwonongeko inandiopsa kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti mafunde a imfa anandizinga, Mitsinje ya zopanda pace inandiopsa ine.