2 Samuel 22:50 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Chifukwa cha zimenezi ndidzakuyamikani Inu Chauta, pakati pa mitundu ya anthu, ndidzaimba nyimbo zotamanda dzina lanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ndidzakuongani Yehova, pakati pa amitundu, ndipo ndidzaimba zolemekeza dzina lanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho ine ndidzakutamandani Inu Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina; ndidzayimba nyimbo zotamanda dzina lanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ndidzakuongani Yehova, pakati pa amitundu, Ndipo ndidzayimba zolemekeza dzina lanu.