2 Samuel 22:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Nthambo zakumanda zidandizeŵeza, misampha ya imfa idandikola.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zingwe za kumanda zinandizingira; misampha ya imfa inandifikira ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zingwe za kumanda zinandizingira; Misampha ya imfa inandifikira ine.