2 Samuel 22:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'mphuno mwake munkafuka utsi, m'kamwa mwake munkatuluka moto woononga, makala amoto anali laŵilaŵi kuchokera m'kamwa momwemo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'mphuno mwake munatuluka utsi, ndi moto wotuluka m'kamwa mwake unaononga; makala anayaka nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼmphuno mwake munatuluka utsi; moto wonyeketsa unatuluka mʼkamwa mwake, makala amoto anali lawilawi mʼkamwa mwake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'mphuno mwace munaturuka utsi, Ndi moto woturuka m'kamwa mwace unaononga; Makala anayaka nao.