2 Samuel 7:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma usiku womwewo Chauta adauza Natani kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunali usiku womwewo mau a Yehova anafika kwa Natani, kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Usiku umenewo mawu a Yehova anafika kwa Natani ndipo anati,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunali usiku womwewo mau a Yehova anafika kwa Natani, kuti,