2 Samuel 8:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zimenezonso mfumu Davide adazipereka kwa Chauta pamodzi ndi siliva ndi golide amene adaafunkha kwa anthu a mitundu ina amene adaŵagonjetsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Izi zomwe mfumu Davide anazipatula zikhale za Yehova, pamodzi ndi siliva ndi golide anapatulako za amitundu onse adawagonjetsa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mfumu Davide inapereka zinthu zimenezi kwa Yehova, monga anachitira ndi siliva ndi golide zochokera ku mayiko onse amene anawagonjetsa:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Izi zomwe mfumu Davide anazipatula zikhale za Yehova, pamodzi ndi siliva ndi golidi anapatulako za amitundu onse adawagonjetsa;